Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 3:4 - Buku Lopatulika

Ndipo kulimbika kotere kwa Mulungu tili nako mwa Khristu:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kulimbika kotere kwa Mulungu tili nako mwa Khristu:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu akudziŵa kuti tikunena zimenezi chifukwa Khristu ndiye amatipatsa kulimba mtima kotere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kulimba mtima kumeneku tili nako pamaso pa Mulungu kudzera mwa Khristu.

Onani mutuwo



2 Akorinto 3:4
5 Mawu Ofanana  

Tamvera mau anga tsopano, ndikupangire nzeru, ndi Mulungu akhale nawe; ukhale m'malo mwa anthu kwa Mulungu, nupite nayo milandu kwa Mulungu;


Koma ayamikike Mulungu, amene atitsogolera m'chigonjetso mwa Khristu, namveketsa fungo la chidziwitso chake mwa ife pamalo ponse.


amene tili naye chokhazikika mtima ndi chiyandiko cholimbika, mwa chikhulupiriro cha pa Iye.


pokhulupirira pamenepo, kuti Iye amene anayamba mwa inu ntchito yabwino, adzaitsiriza kufikira tsiku la Yesu Khristu;


Pakuti kutuluka kwa inu kudamveka mau a Ambuye, osati mu Masedoniya ndi Akaya mokha, komatu m'malo monse chikhulupiriro chanu cha kwa Mulungu chidatuluka; kotero kuti sikufunika kwa ife kulankhula kanthu.