Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 2:8 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake ndikupemphani inu kuti mumtsimikizire ameneyo chikondi chanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake ndikupemphani inu kuti mumtsimikizire ameneyo chikondi chanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake ndikukupemphani kuti mumtsimikizirenso kuti mumamkonda ndithu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho ndikukupemphani kuti mutsimikizire chikondi chanu pa iye.

Onani mutuwo



2 Akorinto 2:8
6 Mawu Ofanana  

kotero kwina kuti inu mumkhululukire ndi kumtonthoza, kuti wotereyo akakamizidwe ndi chisoni chochulukacho.


Pakuti chifukwa cha ichi ndalembanso, kuti ndidziwe mayesedwe anu, ngati muli omvera m'zonse.


Pakuti adakuitanani inu, abale, mukhale mfulu; chokhacho musachite nao ufulu wanu chothandizira thupi, komatu mwachikondi chitiranani ukapolo.


Chifukwa chake, monga tili nayo nyengo, tichitire onse chokoma, koma makamaka iwo a pa banja la chikhulupiriro.