Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 27:7 - Buku Lopatulika

Ndipo kuwerenga kwake kwa masiku Davide anakhala ku dziko la Afilisti ndiko chaka chimodzi ndi miyezi inai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kuwerenga kwake kwa masiku Davide anakhala ku dziko la Afilisti ndiko chaka chimodzi ndi miyezi inai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Davide adakhala ku dziko la Afilisti chaka chimodzi ndi miyezi inai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Davide anakhala mʼdziko la Afilisti kwa chaka chimodzi ndi miyezi inayi.

Onani mutuwo



1 Samueli 27:7
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide ndi anthu ake anakwera, nathira nkhondo yovumbulukira pa Agesuri, ndi Agerizi, ndi Aamaleke; pakuti awa ndiwo anthu akale m'dziko lija, njira ya ku Suri kufikira ku dziko la Ejipito.


Ndipo akalonga a Afilisti anati, Ahebri awa achitanji pano? Ndipo Akisi ananena kwa akalonga a Afilisti, Uyu si Davide uja mnyamata wa Saulo, mfumu ya Israele, amene wakhala nane masiku awa kapena zaka izi, ndipo sindinapeza kulakwa mwa iye, kuyambira tsiku lija anaphatikana nane kufikira lero.