Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 22:21 - Buku Lopatulika

Ndipo Abiyatara anadziwitsa Davide kuti Saulo anapha ansembe a Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abiyatara anadziwitsa Davide kuti Saulo anapha ansembe a Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo adauza Davide kuti Saulo adapha ansembe a Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abiatara anawuza Davide kuti Sauli wapha ansembe a Yehova.

Onani mutuwo



1 Samueli 22:21
3 Mawu Ofanana  

Ndipo munthu wako, amene ndidzamleka osamlikha paguwa langa la nsembe, adzatha maso ako, ndi kumvetsa mtima wako chisoni; ndipo obadwa onse a m'banja lako adzamwalira akali biriwiri.


Ndipo mmodzi wa ana a Ahimeleki, mwana wa Ahitubi, dzina lake ndiye Abiyatara, anapulumuka, nathawira kwa Davide.


Ndipo Davide anati kwa Abiyatara, Tsiku lija Doegi wa ku Edomu anali kumeneko, ndinadziwiratu kuti adzauzadi Saulo; ine ndinafetsa anthu onse a nyumba ya atate wako.