Ndipo munthu wako, amene ndidzamleka osamlikha paguwa langa la nsembe, adzatha maso ako, ndi kumvetsa mtima wako chisoni; ndipo obadwa onse a m'banja lako adzamwalira akali biriwiri.
1 Samueli 22:21 - Buku Lopatulika Ndipo Abiyatara anadziwitsa Davide kuti Saulo anapha ansembe a Yehova. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndipo Abiyatara anadziwitsa Davide kuti Saulo anapha ansembe a Yehova. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Ndipo adauza Davide kuti Saulo adapha ansembe a Chauta. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Abiatara anawuza Davide kuti Sauli wapha ansembe a Yehova. |
Ndipo munthu wako, amene ndidzamleka osamlikha paguwa langa la nsembe, adzatha maso ako, ndi kumvetsa mtima wako chisoni; ndipo obadwa onse a m'banja lako adzamwalira akali biriwiri.
Ndipo mmodzi wa ana a Ahimeleki, mwana wa Ahitubi, dzina lake ndiye Abiyatara, anapulumuka, nathawira kwa Davide.
Ndipo Davide anati kwa Abiyatara, Tsiku lija Doegi wa ku Edomu anali kumeneko, ndinadziwiratu kuti adzauzadi Saulo; ine ndinafetsa anthu onse a nyumba ya atate wako.