Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 20:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Yonatani anati kwa Davide, Chilichonse mtima wako, unena ndidzakuchitira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yonatani anati kwa Davide, Chilichonse mtima wako, unena ndidzakuchitira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Yonatani adauza Davide kuti, “Chilichonse chimene unene, ndidzakuchitira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yonatani anawuza Davide kuti, “Chilichonse chimene iwe ukufuna kuti ndichite, ndidzakuchitira.”

Onani mutuwo



1 Samueli 20:4
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide analumbiranso nati, Atate wako adziwatu kuti wandikomera mtima; nati, Yonatani asadziwe ichi, kuti angamve chisoni; koma pali Yehova, ndiponso pali moyo wako, pakati pa ine ndi imfa pali ngati phazi limodzi.


Nati Davide kwa Yonatani, Onani, mawa mwezi ukhala, ndipo ine ndiyenera kupita kukadya kwa mfumu, wosatsala; koma undilole ndikabisale kuthengo, kufikira tsiku lachitatu madzulo ake.