Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 18:2 - Buku Lopatulika

Ndipo Saulo anamtenga tsiku lomwelo, osamlolanso apite kwao kwa atate wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Saulo anamtenga tsiku lomwelo, osamlolanso apite kwao kwa atate wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwakuti adamtenga Davideyo tsiku lomwelo, osamlola kuti abwerere ku banja kwa bambo wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Sauli anamusunga Davideyo kuyambira tsiku limenelo ndipo sanamulole kuti abwerere ku nyumba ya abambo ake.

Onani mutuwo



1 Samueli 18:2
3 Mawu Ofanana  

Koma Davide akamuka kwa Saulo, nabwerera kudzadyetsa nkhosa za atate wake ku Betelehemu.


Pamenepo Yonatani anaitana Davide, namuuza zonsezi. Ndipo Yonatani anafika naye Davide kwa Saulo, iye nakhalanso pamaso pake monga kale.