Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 17:30 - Buku Lopatulika

Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adachoka apo napita kwa wina namufunsa zokhazokhazo. Aliyense adamuyankhanso monga poyamba paja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anamuchokera napita kwa munthu wina ndipo anamufunsa nkhani yomweyo, ndipo anthu anamuyankha iye monga poyamba paja.

Onani mutuwo



1 Samueli 17:30
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?


Ndipo pamene mau adanena Davide anamveka, anawapitiriza kwa Saulo; ndipo iye anamuitana.