Numeri 3:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mayina a ana aamuna a Aaroni anali Nadabu, woyamba kubadwa, Abihu, Eliezara ndi Itamara. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Ndipo maina ao a ana aamuna a Aroni ndi awa: Woyamba Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo maina ao a ana amuna a Aroni ndi awa: Woyamba Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Maina a ana a Aroni naŵa: Nadabu mwana wake wachisamba, Abihu, Eleazara ndi Itamara. Onani mutuwo |