Eksodo 4:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mose anayankha, “Aisraeliwo sakandikhulupirira ndipo sakandimvera. Iwowo adzati, ‘Yehova sanakuonekere iwe.’ ” Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo Mose anayankha nati, Koma taonani, sadzakhulupirira ine, kapena kumvera mau anga; pakuti adzanena, Yehova sanakuonekere iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Mose anayankha nati, Koma taonani, sadzakhulupirira ine, kapena kumvera mau anga; pakuti adzanena, Yehova sanakuonekere iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mose adayankha kuti, “Koma Aisraelewo sakandikhulupirira, kapena kumvera mau anga. Adzati, ‘Chauta sadakuwonekere.’ ” Onani mutuwo |