Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 2:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iye anayankha kuti, “Inde, pita.” Ndipo mtsikanayo anapita nakayitana amayi a mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Ndipo mwana wamkazi wa Farao ananena naye, Pita. Napita namwaliyo, nakaitana amake wa mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo mwana wamkazi wa Farao ananena naye, Pita. Napita namwaliyo, nakaitana amake wa mwanayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 “Chabwino, pita.” Mlongo wakeyo adapita nakaitana amai ake a mwanayo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 2:8
6 Mawu Ofanana  

Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya Yehova adzandisamala.


Kenaka mlongo wake wa mwanayo anafunsa mwana wa Farao kuti, “Ndingapite kukakupezerani mmodzi mwa amayi a Chihebri kuti azikakulererani mwanayu?”


Mwana wa Farao anati, “Tengani mwanayu mukandilerere, ndidzakulipirani.” Mayiyo anatenga mwanayo kukamulera.


Amramu anakwatira Yokobedi mlongo wa abambo ake, amene anabereka Aaroni ndi Mose. Amramu anakhala ndi moyo kwa zaka 137.


“ ‘Tsono pamene ndinkadutsanso ndinaona kuti nthawi yako yomanga banja inakwana. Tsono ndinakufunditsa chovala changa ndi kubisa umaliseche wako. Ndinachita nawe pangano la ukwati ndipo unakhala wanga, akutero Ambuye Wamphamvuzonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa