Danieli 8:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Chaka chachitatu cha ulamuliro wa mfumu Belisazara, Ine Danieli, ndinaonanso masomphenya, ena atatha amene anandionekera poyamba. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Chaka chachitatu cha Belisazara mfumu masomphenya anandionekera kwa ine Daniele, atatha kundionekera oyamba aja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka chachitatu cha Belisazara mfumu masomphenya anandionekera kwa ine Daniele, atatha kundionekera oyamba aja. Onani mutuwo |