Danieli 3:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iwo anati kwa mfumu Nebukadinezara, “Inu mfumu mukhale ndi moyo wautali! Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Anayankha, nati kwa mfumu Nebukadinezara, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anayankha, nati kwa mfumu Nebukadinezara, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire. Onani mutuwo |