Zekariya 1:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Yehova anamyankha mthenga wakulankhula ndi ine mau okoma, mau akutonthoza mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Yehova anamyankha mthenga wakulankhula ndi ine mau okoma, mau akutonthoza mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta anamuyankha mau abwino ndi okondweretsa mngelo amene amalankhula naneyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho Yehova anayankhula mawu abwino ndi achitonthozo kwa mngelo amene ankayankhula nane. Onani mutuwo |