Zekariya 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo wakuima pakati pa mitengo yamchisu anayankha, nati, Awa ndiwo amene Yehova anawatumiza ayendeyende m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo wakuima pakati pa mitengo yamchisu anayankha, nati, Awa ndiwo amene Yehova anawatumiza ayendeyende m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono munthu amene anaima pa timitengo tazitsamba uja anayankha kuti, ‘Ameneŵa ndiwo amene Chauta waŵatuma kuti ayendere dziko lapansi.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pamenepo munthu amene anayima pakati pa mitengo ya mchisu anafotokoza kuti, “Amenewa ndiwo amene Yehova wawatuma kuti ayendere dziko lonse lapansi.” Onani mutuwo |