Zefaniya 2:2 - Buku Lopatulika2 lamulo lisanabale, tsiku lisanapitirire ngati mungu, usanakugwereni mkwiyo waukali wa Yehova, lisanakugwereni tsiku la mkwiyo wa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 lamulo lisanabale, tsiku lisanapitirire ngati mungu, usanakugwereni mkwiyo waukali wa Yehova, lisanakugwereni tsiku la mkwiyo wa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 adani asanakumwazeni ngati mungu, ukali woopsa wa Chauta usanakugwereni, tsiku la mkwiyo wa Chauta lisanakupezeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 isanafike nthawi yachiweruzo, nthawi yanu isanawuluke ngati mungu, usanakufikeni mkwiyo woopsa wa Yehova, tsiku la ukali wa Yehova lisanafike pa inu. Onani mutuwo |