Zefaniya 1:16 - Buku Lopatulika16 tsiku la lipenga ndi lakufuulira mizinda yamalinga, ndi nsanja zazitali za kungodya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 tsiku la lipenga ndi lakufuulira midzi yamlinga, ndi nsanja zazitali za kungodya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsiku limenelo kudzamveka lipenga ndi kufuula kwankhondo, kwa asilikali othira nkhondo mizinda ya malinga ndiponso nsanja zankhondo za Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsiku loliza lipenga ndi la mfuwu wankhondo, tsiku la kugwa kwa mizinda yotetezedwa ndi nsanja za pa ngodya. Onani mutuwo |