Yoweli 3:12 - Buku Lopatulika12 Agalamuke amitundu, nakwerere kuchigwa cha Yehosafati; pakuti ndidzakhala komweko kuweruza amitundu onse ozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Agalamuke amitundu, nakwerere kuchigwa cha Yehosafati; pakuti ndidzakhala komweko kuweruza amitundu onse ozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Anthu a mitundu yonse akonzeke ndipo abwere ku chigwa cha Yehosafati. Pakuti kumeneko ndidzaweruza anthu a mitundu yonse, ochokera ku mbali zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Mitundu ya anthu idzuke; ipite ku Chigwa cha Yehosafati, pakuti kumeneko Ine ndidzakhala ndikuweruza anthu a mitundu yonse yozungulira. Onani mutuwo |