Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoweli 1:20 - Buku Lopatulika

20 Inde nyama zakuthengo zilira kwa Inu; pakuti mitsinje yamadzi yaphwa, ndi moto wapsereza mabusa a m'chipululu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Inde nyama zakuthengo zilira kwa Inu; pakuti mitsinje yamadzi yaphwa, ndi moto wapsereza mabusa a m'chipululu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Nazonso nyama zakuthengo zikulira kwa Inu, chifukwa timitsinje tonse taphwa, ndipo moto wapsereza mabusa akuthengo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ngakhale nyama zakuthengo zikulirira Inu; timitsinje tonse taphwa ndipo moto wapsereza msipu wa kuthengo.

Onani mutuwo Koperani




Yoweli 1:20
9 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika, atapita masiku ena mtsinje udaphwa, popeza munalibe mvula m'dziko.


Ndipo Ahabu anati kwa Obadiya, Kayendere dziko lonse ku zitsime zonse zamadzi, ndi ku mitsinje yonse, kapena tikapeza msipu ndi kusunga moyo wa akavalo ndi nyuru, zingafe nyama zonse.


Amkonzeratu khwangwala chakudya chake ndani, pamenepo ana ake afuulira kwa Mulungu, naulukauluka osowa chakudya?


Misona ya mkango ibangula potsata nyama yao, nifuna chakudya chao kwa Mulungu.


Maso a onse ayembekeza Inu; ndipo muwapatsa chakudya chao m'nyengo zao.


Amene apatsa zoweta chakudya chao, ana a khwangwala alikulira.


Chifukwa cha nthaka yochita ming'alu, pakuti panalibe mvula padziko, olima ali ndi manyazi, afunda mitu yao.


Aneneri amene analipo kale ndisanakhale ine, nimusanakhale inu, ananenera maiko ambiri, ndi mafumu aakulu, za nkhondo, ndi za choipa, ndi za mliri.


Ha! Nyama ziusa moyo, magulu a ng'ombe azimidwa; pakuti zisowa podyera; magulu a nkhosa omwe atha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa