Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:30 - Buku Lopatulika

30 Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Pamene Yesu ankalankhula zimenezi, anthu ambiri adamkhulupirira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Pamene Iye ankayankhula zimenezi, ambiri anamukhulupirira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.


Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


Koma pamene anali mu Yerusalemu pa Paska pachikondwerero, ambiri anakhulupirira dzina lake, pakuona zizindikiro zake zimene anachitazi.


Chifukwa chake, anthu, poona chizindikiro chimene anachita, ananena, kuti, Ameneyo ndiye mneneri ndithu wakudzayo m'dziko lapansi.


Koma ambiri a m'khamu la anthu anakhulupirira Iye; ndipo ananena, Pamene Khristu akadza kodi adzachita zizindikiro zambiri zoposa zimene adazichita ameneyo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa