Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:13 - Buku Lopatulika

13 Chifukwa chake Afarisi anati kwa Iye, Muchita umboni wa Inu nokha; umboni wanu suli woona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Chifukwa chake Afarisi anati kwa Iye, Muchita umboni wa Inu nokha; umboni wanu suli woona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Apo Afarisi adamuuza kuti, “Ukudzichitira wekha umboni. Umboni wakowo ngwosakwanira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Afarisi anamutsutsa Iye nati, “Iwe ukudzichitira umboni wa Iwe mwini, umboni wako siwoona.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anamkulunga Iye m'maso, namfunsa, nati, Talota; anakupanda Iwe ndani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa