Yohane 6:68 - Buku Lopatulika68 Simoni Petro anamyankha Iye, Ambuye, tidzamuka kwa yani? Inu muli nao mau a moyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201468 Simoni Petro anamyankha Iye, Ambuye, tidzamuka kwa yani? Inu muli nao mau a moyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa68 Simoni Petro adati “Ambuye, nanga tingapitenso kwa yani? Muli nawo ndinu mau opatsa moyo wosatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero68 Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. Onani mutuwo |