Yohane 5:45 - Buku Lopatulika45 Musayesa kuti Ine ndidzakunenezani inu kwa Atate; pali wakukunenezani, ndiye Mose, amene inu mumtama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Musayesa kuti Ine ndidzakunenezani inu kwa Atate; pali wakukunenezani, ndiye Mose, amene inu mumtama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Musayese kuti ndine amene ndidzakunenezeni kwa Atate, ai. Wodzakunenezani alipo. Ndi Mose yemwe uja amene inu mumamdalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 “Koma inu musaganize kuti Ine ndidzakunenezani kwa Atate. Wokunenezani ndi Mose, amene inu mwayikapo chiyembekezo chanu. Onani mutuwo |