Yohane 5:42 - Buku Lopatulika42 Koma ndikudziwani inu, kuti mulibe chikondi cha Mulungu mwa inu nokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Koma ndikudziwani inu, kuti mulibe chikondi cha Mulungu mwa inu nokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Koma ndikukudziŵani, mulibe chikondi cha Mulungu mumtima mwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 koma Ine ndikukudziwani. Ndikudziwa kuti mʼmitima mwanu mulibe chikondi cha Mulungu. Onani mutuwo |