Yohane 4:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti ophunzira ake adachoka kunka kumzinda kuti akagule chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti ophunzira ake adachoka kunka kumudzi kuti akagule chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nthaŵiyo nkuti ophunzira ake aja atakagula chakudya mu mzinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 (Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya). Onani mutuwo |