Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:26 - Buku Lopatulika

26 Yesu ananena naye, Ine wakulankhula nawe ndine amene.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Yesu ananena naye, Ine wakulankhula nawe ndine amene.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Yesu adamuuza kuti, “Ndine amene, Ineyo amene ndikulankhula nanu, mai.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:26
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo analamulira ophunzira kuti asauze munthu kuti Iye ndiye Khristu.


Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino?


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene.


Chifukwa chake ndinati kwa inu, kuti mudzafa m'machimo kwa inu, kuti mudzafa m'machimo anu, pakuti ngati simukhulupirira kuti Ine ndine, mudzafa m'machimo anu.


Chifukwa chake Yesu anati, Pamene mutadzamkweza Mwana wa Munthu, pomwepo mudzazindikira kuti Ine ndine, ndipo sindichita kanthu kwa Ine ndekha, koma monga anandiphunzitsa Atate, ndilankhula izi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa