Yohane 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo tsiku lachitatu panali ukwati mu Kana wa mu Galileya; ndipo amake wa Yesu anali komweko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo tsiku lachitatu panali ukwati m'Kana wa m'Galileya; ndipo amake wa Yesu anali komweko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Patapita masiku aŵiri, kunali ukwati ku mudzi wa Kana m'dera la Galileya. Amai ake a Yesu anali komweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pa tsiku lachitatu munali ukwati mu Kana wa ku Galileya. Amayi ake a Yesu anali komweko, Onani mutuwo |