Yohane 19:34 - Buku Lopatulika34 koma mmodzi wa asilikali anamgwaza ndi nthungo m'nthiti yake, ndipo panatuluka pomwepo mwazi ndi madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 koma mmodzi wa asilikali anamgwaza ndi nthungo m'nthiti yake, ndipo panatuluka pomwepo mwazi ndi madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Koma mmodzi mwa asilikali aja adamubaya m'nthiti mwake ndi mkondo, ndipo nthaŵi yomweyo mudatuluka magazi ndi madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Mʼmalo mwake, mmodzi wa asilikaliwo anamubaya Yesu ndi mkondo mʼnthiti, ndipo nthawi yomweyo munatuluka magazi ndi madzi. Onani mutuwo |