Yohane 18:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo Yesu, podziwa zonse zilinkudza pa Iye, anatuluka, nati kwa iwo, Mufuna yani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo Yesu, podziwa zonse zilinkudza pa Iye, anatuluka, nati kwa iwo, Mufuna yani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yesu adaadziŵiratu zonse zimene zinalikudzamugwera. Nchifukwa chake Iye adaima poyera, naŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna yani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yesu, podziwa zonse zimene zimati zichitike kwa Iye, anatuluka ndi kuwafunsa kuti, “Kodi mukufuna ndani?” Onani mutuwo |