Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 18:21 - Buku Lopatulika

21 Undifunsiranji Ine? Funsa iwo amene adamva chimene ndinalankhula nao; taona, amenewo adziwa chimene ndinanena Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Undifunsiranji Ine? Funsa iwo amene adamva chimene ndinalankhula nao; taona, amenewo adziwa chimene ndinanena Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Nanga tsono mukundifunsiranji Ineyo? Funsani amene adamva zomwe ndinkaŵauza. Iwowo akudziŵa zimene ndinkanena.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Nʼchifukwa chiyani mukundifunsa Ine? Afunseni amene amamva. Zoonadi akudziwa zimene Ine ndinanena.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:21
7 Mawu Ofanana  

nanena, Ngati uli Khristu, utiuze. Ndipo anati kwa iwo, Ndikakuuzani, simudzavomereza;


Yesu anayankha iye, Ine ndalankhula zomveka kwa dziko lapansi; ndinaphunzitsa Ine nthawi zonse m'sunagoge ndi mu Kachisi, kumene amasonkhana Ayuda onse; ndipo mobisika sindinalankhule kanthu.


Koma m'mene Iye adanena izi, mmodzi wa anyamata akuimirirako anapanda Yesu khofu, ndi kuti, Kodi uyankha mkulu wa ansembe chomwecho?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa