Yohane 17:25 - Buku Lopatulika25 Atate wolungama, dziko lapansi silinadziwe Inu, koma Ine ndinadziwa Inu; ndipo iwo anazindikira kuti munandituma Ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Atate wolungama, dziko lapansi silinadziwa Inu, koma Ine ndinadziwa Inu; ndipo iwo anazindikira kuti munandituma Ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Atate olungama, anthu odalira zapansipano sadakudziŵeni ai, koma Ine ndimakudziŵani, ndipo aŵa ali panoŵa akudziŵa kuti ndinu mudandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 “Atate wolungama, ngakhale kuti dziko lapansi silikudziwani Inu, Ine ndimakudziwani, ndipo iwo amadziwa kuti Inu munandituma Ine. Onani mutuwo |