Yohane 15:3 - Buku Lopatulika3 Mwakhala okonzeka tsopano inu chifukwa cha mau amene ndalankhula ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mwakhala okonzeka tsopano inu chifukwa cha mau amene ndalankhula ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Inu mwayera kale chifukwa cha mau amene ndakuuzani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu. Onani mutuwo |