Yohane 14:18 - Buku Lopatulika18 Sindidzakusiyani inu mukhale ana amasiye; ndidza kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Sindidzakusiyani inu mukhale ana amasiye; ndidza kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Sindidzakusiyani nokha kuti mukhale ana amasiye. Ndidzabweranso kwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ine sindikusiyani nokha kuti mukhale ana amasiye. Ine ndidzabweranso kwa inu. Onani mutuwo |