Yohane 12:25 - Buku Lopatulika25 Iye wokonda moyo wake adzautaya; ndipo wodana ndi moyo wake m'dziko lino lapansi adzausungira kumoyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Iye wokonda moyo wake adzautaya; ndipo wodana ndi moyo wake m'dziko lino lapansi adzausungira kumoyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Munthu amene amakonda moyo wake, adzautaya, koma amene saikapo mtima pa moyo wake pansi pano, adzausungira ku moyo wosatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. Onani mutuwo |