Yohane 10:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa cha ichi Atate andikonda Ine, chifukwa nditaya Ine moyo wanga, kuti ndikautengenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa cha ichi Atate andikonda Ine, chifukwa nditaya Ine moyo wanga, kuti ndikautengenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Nchifukwa chake Atate amandikonda, popeza kuti ndikupereka moyo wanga kuti ndikautengenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Nʼchifukwa chake Atate anga amandikonda, popeza Ine ndikupereka moyo wanga kuti ndiwutengenso. Onani mutuwo |