Yohane 1:13 - Buku Lopatulika13 amene sanabadwe ndi mwazi, kapena ndi chifuniro cha thupi, kapena ndi chifuniro cha munthu, koma cha Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 amene sanabadwe ndi mwazi, kapena ndi chifuniro cha thupi, kapena ndi chifuniro cha munthu, koma cha Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kukhala ana a Mulungu kumeneku sikudachokere m'kubadwa kwao, kapena ku chifuniro cha thupi, kapena ku chifuniro cha munthu ai, koma kudachokera kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 ana wobadwa osati monga mwachilengedwe, kapena chisankho cha munthu, kapena chifuniro cha mwamuna koma wobadwa mwa Mulungu. Onani mutuwo |