Yeremiya 7:8 - Buku Lopatulika8 Taonani, mukhulupirira mau onama, osapindulitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Taonani, mukhulupirira mau onama, osapindulitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Koma onani, inu mumakhulupirira mabodza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma onani, inu mukudalira mawu abodza amene alibe phindu. Onani mutuwo |