Yeremiya 51:57 - Buku Lopatulika57 Ndipo ndidzaledzeretsa akulu ake ndi anzeru ake, akazembe ake ndi ziwanga zake, ndi anthu ake olimba; ndipo adzagona chigonere, sadzanyamuka, ati Mfumu, dzina lake ndi Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 Ndipo ndidzaledzeretsa akulu ake ndi anzeru ake, akazembe ake ndi ziwanga zake, ndi anthu ake olimba; ndipo adzagona chigonere, sadzanyamuka, ati Mfumu, dzina lake ndi Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Ndidzaledzeretsa akuluakulu ake pamodzi ndi anzeru ake. Ndidzaledzeretsa abwanamkubwa ake, atsogoleri ankhondo, ndi ankhondo ake amene. Adzagona tulo tampakampaka, tosadzuka nato,” ikutero mfumu imene dzina lake ndi Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Ndidzaledzeretsa akuluakulu ake pamodzi ndi anzeru ake, abwanamkubwa ake, atsogoleri a ankhondo pamodzinso ndi ankhondo; adzagona kwamuyaya osadzukanso,” akutero Mfumu, amene dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |