Yeremiya 38:3 - Buku Lopatulika3 Yehova atero, Mzindawu udzapatsidwatu m'dzanja la nkhondo ya mfumu ya ku Babiloni, ndipo adzaulanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yehova atero, Mudziwu udzapatsidwatu m'dzanja la nkhondo ya mfumu ya ku Babiloni, ndipo adzaulanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mzinda uno udzaperekedwadi kwa ankhondo a mfumu ya ku Babiloni, ndipo adzaulanda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mzinda uno udzaperekedwa ndithu kwa gulu lankhondo la mfumu ya ku Babuloni, amene adzawulande.’ ” Onani mutuwo |