Yeremiya 27:4 - Buku Lopatulika4 nuwauze iwo anene kwa ambuyao, kuti, Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero: Muzitero kwa ambuyanu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nuwauze iwo anene kwa ambuyao, kuti, Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero: Muzitero kwa ambuyanu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Uŵauze kuti akadziŵitse atsogoleri ao kuti Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israele, akuuza atsogoleriwo kuti: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Uwapatse uthenga wokapereka kwa ambuye awo ndipo uwawuze kuti: Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Mukawuze ambuye anu kuti: Onani mutuwo |