Yeremiya 26:1 - Buku Lopatulika1 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, panadza mau awa ochokera kwa Yehova, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, panadza mau awa ochokera kwa Yehova, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Yehoyakimu, mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda, adayamba kulamulira, Chauta adauza Yeremiya kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehoyakimu, mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda atayamba kulamulira, Yehova anayankhula ndi Yeremiya kuti, Onani mutuwo |