Yeremiya 23:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo ndidzasonkhanitsa zotsala za zoweta zanga za m'maiko onse m'mene ndinazipirikitsiramo, ndipo ndidzazitengeranso kumakola ao; ndipo zidzabalana ndi kuchuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo ndidzasonkhanitsa zotsala za zoweta zanga za m'maiko onse m'mene ndinazipirikitsiramo, ndipo ndidzazitengeranso kumakola ao; ndipo zidzabalana ndi kuchuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pambuyo pake Mwiniwakene ndidzasonkhanitsa nkhosa zanga zotsala, kuzichotsa ku malo onse amene ndidazimwazira. Ndidzazibwezera ku busa lakwao, ndipo zidzaswana ndi kuchuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Pambuyo pake Ine mwini wakene ndidzasonkhanitsa nkhosa zanga zotsala, kuzichotsa ku mayiko onse kumene ndinazibalalitsira ndi kuzibweretsanso ku msipu wawo. Kumeneko zidzaswana ndi kuchulukana. Onani mutuwo |