Yeremiya 2:34 - Buku Lopatulika34 Ndiponso m'nsalu zako wapezeka mwazi wa miyoyo ya aumphawi osachimwa; sunawapeze pakuboola, koma ponsepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndiponso m'nsalu zako wapezeka mwazi wa miyoyo ya aumphawi osachimwa; sunawapeza pakuboola, koma ponsepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Zovala zanu zili psu ndi magazi a anthu osauka osachimwa. Anthuwo simudaŵapeze nathyola nyumba. Komabe, ngakhale zinthu zili choncho, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Ngakhale pa zovala zako anthu amapezapo magazi a anthu osauka osalakwa. Anthuwo simunawapeze akuthyola nyumba. Komabe ngakhale zinthu zili chomwechi, Onani mutuwo |