Yeremiya 2:2 - Buku Lopatulika2 Pita nufuule m'makutu a Yerusalemu, kuti, Yehova atero, Ndikumbukira za iwe kukoma mtima kwa ubwana wako, chikondi cha matomedwe ako; muja unanditsata m'chipululu m'dziko losabzalamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pita nufuule m'makutu a Yerusalemu, kuti, Yehova atero, Ndikumbukira za iwe kukoma mtima kwa ubwana wako, chikondi cha matomedwe ako; muja unanditsata m'chipululu m'dziko losabzalamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 ndikalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu mau ake akuti, “Ndikukumbukira m'mene munkakhulupirikira pa unyamata wanu, m'mene poyamba paja munkandikondera monga amachitira mkwati wamkazi. Mudanditsata m'chipululu, m'dziko losabzalamo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Pita ukalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu kuti Yehova akuti, “ ‘Ine ndikukumbukira mmene umakhulupirikira pa unyamata wako, mmene unkandikondera ngati momwe amachitira mkwatibwi, mmene unkanditsata mʼchipululu muja; mʼdziko losadzalamo kanthu. Onani mutuwo |