Yeremiya 10:4 - Buku Lopatulika4 Aukometsa ndi siliva ndi golide; auchirikiza ndi misomali ndi nyundo, kuti usasunthike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Aukometsa ndi siliva ndi golide; auchirikiza ndi misomali ndi nyundo, kuti usasunthike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Anthu ena amakongoletsa chosemacho ndi siliva ndi golide, kenaka nkuchikhomerera ndi misomali, kuti chisagwedezeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amakongoletsa chosemacho ndi siliva ndi golide; kenaka amachikhomerera ndi misomali kuti chisagwedezeke. Onani mutuwo |