Yeremiya 1:8 - Buku Lopatulika8 Usaope nkhope zao; chifukwa Ine ndili ndi iwe kuti ndikulanditse iwe, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Usaope nkhope zao; chifukwa Ine ndili ndi iwe kuti ndikulanditse iwe, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Usaŵaope, Ine ndili nawe, ndidzakupulumutsa,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Usawaope, pakuti Ine ndili nawe, ndipo ndidzakupulumutsa,” akutero Yehova. Onani mutuwo |