Yeremiya 1:1 - Buku Lopatulika1 Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Aŵa ndi mau a Yeremiya, mwana wa Hilikiya, mmodzi mwa ansembe a ku Anatoti, m'dziko la Benjamini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mawu a Yeremiya mwana wa Hilikiya, mmodzi mwa ansembe a ku Anatoti, mʼdziko la Benjamini. Onani mutuwo |