Yakobo 5:1 - Buku Lopatulika1 Nanga tsono achuma inu, lirani ndi kuchema chifukwa cha masautso anu akudza pa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Nanga tsono achuma inu, lirani ndi kuchema chifukwa cha masautso anu akudza pa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mverani tsono, inu anthu achumanu. Lirani ndi kufuula chifukwa cha zovuta zimene zikudzakugwerani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono tamverani, inu anthu achuma, lirani ndi kufuwula chifukwa cha zovuta zimene zidzakugwereni. Onani mutuwo |