Yakobo 4:7 - Buku Lopatulika7 Potero mverani Mulungu; koma kanizani mdierekezi, ndipo adzakuthawani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Potero mverani Mulungu; koma kanizani mdierekezi, ndipo adzakuthawani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono muzigonjera Mulungu. Satana muzilimbana naye, ndipo adzakuthaŵani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Dziperekeni nokha kwa Mulungu. Mukaneni Mdierekezi ndipo adzakuthawani. Onani mutuwo |
kuti adzakuingitsani kukuchotsani kwa anthu, ndi pokhala panu padzakhala pamodzi ndi nyama zakuthengo; ndipo mudzadya udzu ngati ng'ombe, nimudzakhala wokhathamira ndi mame a kumwamba, ndipo zidzakupitirani nthawi zisanu ndi ziwiri, mpaka mudzadziwa kuti Wam'mwambamwamba alamulira mu ufumu wa anthu, naupereka kwa aliyense Iye afuna mwini.