Yakobo 4:5 - Buku Lopatulika5 Kodi muyesa kapena kuti malembo angonena chabe? Kodi Mzimuyo adamkhalitsa mwa ife akhumbitsa kuchita nsanje? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Kodi muyesa kapena kuti malembo angonena chabe? Kodi Mzimuyo adamkhalitsa mwa ife akhumbitsa kuchita nsanje? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kodi kapena mukuyesa kuti Malembo amanena pachabe kuti, “Mulungu amafunitsitsa mwansanje mzimu umene Iye adaika kuti uzikhala mwa ife?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kapena mukuganiza kuti Malemba amanena popanda chifukwa kuti Mulungu amafunitsitsa mwansanje mzimu umene Iye anayika kuti uzikhala mwa ife? Onani mutuwo |