Yakobo 3:3 - Buku Lopatulika3 Koma ngati tiikira akavalo zogwirira m'kamwa mwao atimvere, tipotolozanso thupi lao lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma ngati tiikira akavalo zogwirira m'kamwa mwao atimvere, tipotolozanso thupi lao lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Timaika kachitsulo m'kamwa mwa kavalo kuti atimvere, ndipo tingathe kumaongolera thupi lake lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tikayika tizitsulo mʼkamwa mwa akavalo kuti atimvere, timatha kuwongolera thupi lake lonse. Onani mutuwo |